is a project which YONECO is implementing in Machinga and Zomba, with financial support from Foundation S. The project aims to strengthen the climate resilience of communities by enabling people to better prepare for, cope with, and manage the health risks posed by climate variability and change. #CommunityResilience #ClimateAction #HealthForAll
Read MoreTiyeni titenge mbali pothetsa nkhanza kwa amai ndi ana poneneza anthu omwe amachita nkhanzazi poyimba foni mwaulere pa 5600 #SDG5 #16DaysofActivism #endGBV
Read MoreMuvi oyang’anira suchedwa kulowa mmaso. Nkhaza zimabweretsa mabvuto osiyanasiyana. Tiyeni tiulure nkhazazi kwa adindo. Kapena kuyimba foni mwaulere pa 5600. #SDG5 #16DaysofActivism #endGBV
Read MoreNkhanza tikazilekelera zimabala mavuto aakulu. Tiyeni tisachitire ena nkhanza, koma tikondane ndikutetezana wina ndi nzake. #SDG5 #16DaysofActivism #endGBV
Read MoreTiyeni tiwazindikiritse ana anthu nkhanza zomwe angakumanenazo ndikuwalimbikitsa kuti adziulura akachitilidwa nkhanzazi. #SDG5 #16DaysofActivism #endGBV
Read MoreNkhanza zimabwezera chitikuko pambuyo. Atsogoleri ndi udindo wathu kuthetsa nkhanza zochitika chifukwa wina ndi mamuna kapena mkazi. #SDG5 #16DaysofActivism #endGBV
Read MoreNane Ndimafuna ndizakhale pomwe mulipo. Musandichite nkhanza koma ndithandizeni kukwaniritsa maloto anga. #SDG5 #16DaysofActivism #endGBV
Read MoreAdindo, limbikitsani ntchito yoteteza ufulu wa amayi ndi ana munthawi ya ngozi zogwa mwadzidzi. #SDG5 #16DaysofActivism #endGBV
Read MoreMakolo onetsetsani kuti mukuwamasukira ana anu kunkhani zogonana kuwopa kuuzidwa zosayenera ndi amzawo. #SDG5 #16DaysofActivism #endGBV
Read More
